Yeremiya 18:23 - Buku Lopatulika23 Koma, Yehova, mudziwa uphungu wao wonse wakundinenera ine kundipha ine; musakhulukire mphulupulu yao, musafafanize tchimo lao pamaso panu; aphunthwitsidwe pamaso panu; muchite nao m'nthawi ya mkwiyo wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma, Yehova, mudziwa uphungu wao wonse wakundinenera ine kundipha ine; musakhulukire mphulupulu yao, musafafanize tchimo lao pamaso panu; aphunthwitsidwe pamaso panu; muchite nao m'nthawi ya mkwiyo wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Inu Chauta, mukudziŵadi ziwembu zao zonse zofuna kundipha. Musaŵakhululukire zolakwa zao, ndithu, musaŵachotsere machimo ao. Agonjetsedwe pamaso panu, ndipo muŵalange muli okwiya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Koma Inu Yehova, mukudziwa ziwembu zawo zonse zofuna kundipha. Musawakhululukire zolakwa zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu. Agonjetsedwe pamaso panu; muwalange muli wokwiya.” Onani mutuwo |