Yeremiya 18:22 - Buku Lopatulika22 Mfuu umvekedwe m'nyumba zao, pamene muwatengera khamu la nkhondo dzidzidzi; pakuti akumba dzenje lakundigwira ine, anabisira mapazi anga misampha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Mfuu umvekedwe m'nyumba zao, pamene muwatengera khamu la nkhondo dzidzidzi; pakuti akumba dzenje lakundigwira ine, anabisira mapazi anga misampha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Muŵatumire gulu lankhondo lidzaŵakanthe modzidzimutsa, ndipo kulira kwamantha kumveke m'nyumba zao. Iwotu andikumbira dzenje loti andiponyemo, ndipo atchera mapazi anga msampha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kulira kumveke kuchokera mʼnyumba zawo mutawatumizira gulu lankhondo mwadzidzidzi kuti liwakanthe. Iwo andikumbira dzenje kuti ndigweremo ndipo atchera msampha mapazi anga. Onani mutuwo |