Yeremiya 18:14 - Buku Lopatulika14 Kodi matalala a Lebanoni adzalephera pamwala wa m'munda? Kodi adzaphwa madzi ozizira otsika kutali? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Kodi matalala a Lebanoni adzalephera pa mwala wa m'munda? Kodi adzaphwa madzi ozizira otsika kutali? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kodi chisanu chimatha pa mathanthwe otsetsereka a phiri la Lebanoni? Kodi mitsinje ya madzi ozizira ochokera ku phiri la Lebanoni imaphwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kodi chisanu chimatha pa matanthwe otsetsereka a phiri la Lebanoni? Kodi madzi ozizira amitsinje ochokera ku phiri la Lebanoni adzamphwa? Onani mutuwo |