Yeremiya 18:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake atero Yehova; Funsanitu m'mitundu, ndani wamva zotero; namwali wa Israele wachita chinthu choopsetsa kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake atero Yehova; Funsanitu m'mitundu, ndani wamva zotero; namwali wa Israele wachita chinthu choopsetsa kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nchifukwa chake Chauta akunena kuti, “Ukafunse anthu a mitundu ina yonse, ngati alipo amene adamvapo zotere. Israele amene adaali ngati namwali wosadziŵa mwamuna wachita chinthu choipa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yehova akuti, “Uwafunse anthu a mitundu ina kuti: Kodi ndani anamvapo zinthu zofanana ndi zimenezi? Israeli amene anali ngati namwali wanga wachita chinthu choopsa kwambiri. Onani mutuwo |