Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 18:1 - Buku Lopatulika

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anawuza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 18:1
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Ozolitsa inu! Kodi woumba adzayesedwa ngati dothi; kodi chinthu chopangidwa chinganene za iye amene anachipanga, Iye sanandipange ine konse; kapena kodi chinthu choumbidwa chinganene za iye amene anachiumba, Iye alibe nzeru?


Koma ngati simudzamvera Ine kulipatula tsiku la Sabata, kusanyamula katundu ndi kulowa pa zipata za Yerusalemu tsiku la Sabata; pamenepo ndidzayatsa moto m'zipata zakezo, ndipo udzatha zinyumba za Yerusalemu, osazimidwanso.


Tauka, tatsikira kunyumba ya woumba, pamenepo ndidzakumvetsa mau anga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa