Yeremiya 17:23 - Buku Lopatulika23 koma sanamvere, sanatchere khutu lao, koma anaumitsa khosi lao, kuti asamve asalandire langizo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 koma sanamvere, sanatchere khutu lao, koma anaumitsa khosi lao, kuti asamve asalandire langizo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Iwowo sadamvere kapena kusamalako, koma ndi mitima yokanika adakana kumva ndi kulandira malangizo anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Komatu iwo sanandimvere kapena kulabadira. Ndi mitima yawo yowumayo sanamvere kapena kulandira malangizo anga. Onani mutuwo |