Yeremiya 17:21 - Buku Lopatulika21 atero Yehova: Tadzayang'anirani nokha, musanyamule katundu tsiku la Sabata, musalowe naye pa zipata za Yerusalemu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 atero Yehova: Tadzayang'anirani nokha, musanyamule katundu tsiku la Sabata, musalowe naye pa zipata za Yerusalemu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 M'mau a Chautawo ndi aŵa: Kuti musunge moyo wanu, samalani bwino kuti pa tsiku la Sabata musanyamule katundu, kapena kuloŵa naye pa zipata za Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yehova akuti: samalani kuti pa tsiku la Sabata musanyamule katundu kapena kulowa naye pa zipata za Yerusalemu. Onani mutuwo |