Yeremiya 17:13 - Buku Lopatulika13 Inu Yehova, chiyembekezo cha Israele, onse amene akukusiyani Inu adzakhala ndi manyazi; onse ondichokera Ine adzalembedwa m'dothi, chifukwa asiya Yehova, kasupe wa madzi amoyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Inu Yehova, chiyembekezo cha Israele, onse amene akukusiyani Inu adzakhala ndi manyazi; onse ondichokera Ine adzalembedwa m'dothi, chifukwa asiya Yehova, kasupe wa madzi amoyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu Chauta, amene Aisraele amagonera pa Inu, onse okukanani adzaŵachititsa manyazi. Onse okusiyani adzafafanizika ngati maina olembedwa pa dothi, chifukwa chokana Chauta, kasupe wa madzi opatsa moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Inu Yehova, chiyembekezo cha Israeli, onse amene amakusiyani adzachita manyazi. Iwo amene amakufulatirani mayina awo adzafafanizika ngati olembedwa pa fumbi chifukwa anakana Yehova, kasupe wa madzi amoyo. Onani mutuwo |