Yeremiya 16:8 - Buku Lopatulika8 Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Usadzaloŵe m'nyumba m'mene muli phwando, kuti udye nao ndi kumwa nao,” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Ndipo usalowe mʼnyumba mmene muli madyerero, nʼkukhala pansi ndi kudya ndi kumwa nawo. Onani mutuwo |