Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 16:8 - Buku Lopatulika

8 Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 “Usadzaloŵe m'nyumba m'mene muli phwando, kuti udye nao ndi kumwa nao,”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “Ndipo usalowe mʼnyumba mmene muli madyerero, nʼkukhala pansi ndi kudya ndi kumwa nawo.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 16:8
9 Mawu Ofanana  

Sindinakhala pansi ndi anthu achabe; kapena kutsagana nao anthu othyasika.


Sindinakhala m'msonkhano wa iwo amene asekerasekera, ndi kusangalala; ndinakhala pandekha chifukwa cha dzanja lanu; pakuti mwandidzaza ndi mkwiyo.


Pakuti monga m'masiku aja, chisanafike chigumula, anthu analinkudya ndi kumwa, analikukwatira ndi kukwatiwa, kufikira tsiku limene Nowa analowa m'chingalawa,


koma tsopano ndalembera inu kuti musayanjane naye, ngati wina wotchedwa mbale ali wachigololo, kapena wosirira, kapena wopembedza mafano, kapena wolalatira, kapena woledzera, kapena wolanda, kungakhale kukadya naye wotere, iai.


ndipo musayanjane nazo ntchito za mdima zosabala kanthu, koma makamakanso muzitsutse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa