Yeremiya 16:7 - Buku Lopatulika7 anthu sadzawagawira mkate pamaliro, kuti atonthoze mitima yao chifukwa cha akufa, anthu sadzapatsa iwo chikho cha kutonthoza kuti achimwe chifukwa cha atate ao kapena mai wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 anthu sadzawagawira mkate pamaliro, kuti atonthoze mitima yao chifukwa cha akufa, anthu sadzapatsa iwo chikho cha kutonthoza kuti achimwe chifukwa cha atate ao kapena mai wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Palibe amene adzapatse chakudya munthu wolira kuti amtonthoze chifukwa cha akufawo. Sadzamupatsa chakumwa kuti amtonthoze, ngakhale amwalire atate ake kapena amai ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Palibe amene adzapereka chakudya kutonthoza amene akulira maliro, ngakhale kuti womwalirayo ndi abambo ake kapena amayi ake. Onani mutuwo |