Yeremiya 16:12 - Buku Lopatulika12 ndipo mwachita zoipa zopambana makolo anu; pakuti, taonani, muyenda yense potsata kuumirira kwa mtima wake woipa, kuti musandimvere Ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndipo mwachita zoipa zopambana makolo anu; pakuti, taonani, muyenda yense potsata kuumirira kwa mtima wake woipa, kuti musandimvere Ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Komanso inu mudachimwa koposa kupambana makolo anu: aliyense mwa inu akutsata zoipa ndi mtima wake wokanika, m'malo momandimvera Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Komanso inu munachimwa kwambiri kupambana makolo anu. Aliyense wa inu akutsatira zoyipa ndi mtima wake wokanikawo mʼmalo mondimvera Ine. Onani mutuwo |