Yeremiya 16:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo padzakhala, pamene udzaonetsa anthu awa mau awa onse, ndipo iwo adzati kwa iwe, Chifukwa chake nchiyani kuti Yehova watinenera ife choipa chachikulu ichi? Mphulupulu yathu ndi yanji? Tchimo lathu lanji limene tachimwira Yehova Mulungu wathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo padzakhala, pamene udzaonetsa anthu awa mau awa onse, ndipo iwo adzati kwa iwe, Chifukwa chake nchiyani kuti Yehova watinenera ife choipa chachikulu ichi? Mphulupulu yathu ndi yanji? Tchimo lathu lanji limene tachimwira Yehova Mulungu wathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Tsono ukadzaŵauza anthuwo mau ameneŵa, makamaka adzakufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani Chauta wanena kuti tsoka lotere lidzatigwera ifeyo? Kodi tidalakwanji? Kodi Inu Chauta, Mulungu wathu, takuchimwirani chiyani?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Ukawawuza anthu awa zinthu zonsezi akakufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani Yehova wanena kuti tsoka lalikulu lotere lidzatigwere? Kodi talakwa chiyani? Kodi tamuchimwira tchimo lotani Yehova Mulungu wathu?’ Onani mutuwo |