Yeremiya 15:8 - Buku Lopatulika8 Amasiye ao andichulukira Ine kopambana mchenga wa kunyanja; ndatengera wofunkha usana afunkhire mai wao wa anyamata; ndamgwetsera dzidzidzi kuwawa mtima ndi mantha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Amasiye ao andichulukira Ine kopambana mchenga wa kunyanja; ndatengera wofunkha usana afunkhire mai wao wa anyamata; ndamgwetsera dzidzidzi kuwawa mtima ndi mantha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Akazi amasiye ndidaŵachulukitsa, kupambana mchenga wakunyanja. Amai ndidaŵaonongera ana ao akali anyamata abiriŵiri. Mwadzidzidzi ndidaŵagwetsera chisoni ndi nkhaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndinachulukitsa amayi awo amasiye kupambana mchenga wa kunyanja. Amayiwo ndinawawonongera ana awo aamuna dzuwa lili pamutu. Mwadzidzidzi ndinawagwetsera kuwawa mtima ndi mantha. Onani mutuwo |