Yeremiya 15:7 - Buku Lopatulika7 Ndawapeta ndi chopetera m'zipata za dziko; ndachotsa ana ao, ndasakaza anthu anga; sanabwerere kuleka njira zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndawapeta ndi chopetera m'zipata za dziko; ndachotsa ana ao, ndasakaza anthu anga; sanabwerere kuleka njira zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndidaŵabalalitsira uku ndi uku, monga momwe amachitira ndi mankhusu popeta ndi lichero. Ndidaŵaliritsa anthu anga ndi kuŵaononga, chifukwa sadafune kusiya makhalidwe ao oipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ine ndidzakubalalitsani kukuchotsani mʼmizinda ya mʼdzikomo monga mmene amachitira ndi mankhusu popeta ndi lichero. Anthu anga ndinawaliritsa ndi kuwawononga chifukwa sanasinthe makhalidwe awo oyipa. Onani mutuwo |