Yeremiya 15:18 - Buku Lopatulika18 Kupweteka kwanga kuli chipwetekere bwanji, ndi bala langa losapoleka, likana kupola? Kodi mudzakhala kwa ine ngati kamtsinje konyenga, ngati madzi omwerera? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Kupweteka kwanga kuli chipwetekere bwanji, ndi bala langa losapoleka, likana kupola? Kodi mudzakhala kwa ine ngati kamtsinje konyenga, ngati madzi omwerera? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nanga chifukwa chiyani mavuto anga sakutha? Chilonda changa nchosatha, sichikupola. Monga nkuti mwandinyenga ngati chitsime chouma kapena ngati mtsinje wopanda madzi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nanga nʼchifukwa chiyani mavuto anga sakutha? Bwanji chilonda changa sichikupola? Kodi inu mudzakhala ngati mtsinje wowuma nthawi yachilimwe, kapena ngati kasupe wopanda madzi?” Onani mutuwo |