Yeremiya 15:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo ndidzawapititsa iwo pamodzi ndi adani ako kudziko limene sudziwa iwe; pakuti moto wayaka m'mkwiyo wanga, umene udzatentha inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo ndidzawapititsa iwo pamodzi ndi adani ako kudziko limene sudziwa iwe; pakuti moto wayaka m'mkwiyo wanga, umene udzatentha inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndidzakusandutsani akapolo a adani anu m'dziko limene simulidziŵa. Ndithudi, mkwiyo wanga wayaka, ndipo udzakutenthani kosalekeza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndidzakusandutsani akapolo a adani anu mʼdziko limene inu simulidziwa, chifukwa mkwiyo wanga wayaka ngati moto umene udzakutenthani.” Onani mutuwo |