Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 15:12 - Buku Lopatulika

12 Kodi angathe munthu kuthyola chitsulo, chitsulo cha kumpoto, ndi mkuwa?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Kodi angathe munthu kuthyola chitsulo, chitsulo cha kumpoto, ndi mkuwa?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Kodi munthu angathe kudula chitsulo, chitsulo chochokera kumpoto chosakaniza ndi mkuŵa?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Palibe munthu amene angathe kudula chitsulo, makamaka chitsulo chochokera kumpoto chosakaniza ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 15:12
7 Mawu Ofanana  

Kodi uli nalo dzanja ngati Ine Mulungu? Kapena ukhoza kugunda ndi mau ngati Ine?


Tsoka kwa iye amene akangana ndi Mlengi wake! Phale mwa mapale a dziko lapansi! Kodi dongo linganene kwa iye amene aliumba, Kodi upanga chiyani? Pena ntchito yako, Iye alibe manja?


Pakuti atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Ndaika goli lachitsulo pa khosi la amitundu onsewa, kuti amtumikire Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni; ndipo adzamtumikira iye; ndipo ndampatsanso nyama zakuthengo.


Malire anu a kumpoto ndiwo: kuyambira ku Nyanja Yaikulu mulinge kuphiri la Hori:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa