Yeremiya 15:11 - Buku Lopatulika11 Yehova anati, Ndithu ndidzakulimbitsira iwe zabwino; ndithu ndidzapembedzetsa mdani kwa iwe nthawi ya zoipa ndi nthawi ya nsautso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova anati, Ndithu ndidzakulimbitsira iwe zabwino; ndithu ndidzapembedzetsa mdani kwa iwe nthawi ya zoipa ndi nthawi ya nsautso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adayankha kuti, “Koma zoonadi ndidzakulanditsa kuti upeze bwino. Ndithudi, adani ako adzakupemba pa nthaŵi ya tsoka ndi ya mavuto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova anati, “Ndithudi, Ine ndidzakulanditsa kuti upeze bwino. Ndithudi, adani ako adzakupempha pa nthawi ya tsoka ndi ya mavuto awo. Onani mutuwo |