Yeremiya 14:9 - Buku Lopatulika9 Bwanji mukhala ngati munthu wodabwa, ngati munthu wamphamvu wosatha kupulumutsa? Koma Inu, Yehova, muli pakati pathu, titchedwa ndi dzina lanu; musatisiye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Bwanji mukhala ngati munthu wodabwa, ngati munthu wamphamvu wosatha kupulumutsa? Koma Inu, Yehova, muli pakati pathu, titchedwa ndi dzina lanu; musatisiye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa chiyani mukukhala ngati munthu wothedwa nzeru? Mukukhaliranji ngati wankhondo amene sangathenso kupulumutsa anthu? Komabe Inu Chauta, muli pakati pathu, ife amene timadziŵika ndi dzina lanu, choncho musatisiye tokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Chifukwa chiyani muli ngati munthu amene wadzidzimutsidwa, kapena ngati wankhondo amene alibe mphamvu yopulumutsa? Komabe Inu Yehova, muli pakati pathu, ndipo tikudziwika ndi dzina lanu; musatitaye ife!” Onani mutuwo |