Yeremiya 14:8 - Buku Lopatulika8 Inu, chiyembekezo cha Israele, Mpulumutsi wake nthawi ya msauko, bwanji mukhala ngati mlendo m'dziko, ngati woyendayenda amene apatuka usiku? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Inu, chiyembekezo cha Israele, Mpulumutsi wake nthawi ya msauko, bwanji mukhala ngati mlendo m'dziko, ngati woyendayenda amene apatuka usiku? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu Chauta, amene muli chikhulupiriro cha Aisraele, ndiponso Mpulumutsi wao pa nthaŵi ya mavuto, mukukhaliranji ngati mlendo m'dziko lino, ngati wapaulendo wogona usiku umodzi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu Yehova amene Aisraeli amakukhulupirirani ndi amene mumawapulumutsa pa nthawi ya masautso, chifukwa chiyani mukukhala ngati mlendo mʼdziko muno? Chifukwa chiyani muli ngati wapaulendo amene akungogona tsiku limodzi? Onani mutuwo |