Yeremiya 14:7 - Buku Lopatulika7 Zingakhale zoipa zathu zititsutsa ife, chitani Inu chifukwa cha dzina lanu, Yehova; pakuti zobwerera zathu zachuluka; takuchimwirani Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Zingakhale zoipa zathu zititsutsa ife, chitani Inu chifukwa cha dzina lanu, Yehova; pakuti zobwerera zathu zachuluka; takuchimwirani Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthu akuti, “Inu Chauta, ngakhale machimo athu akutipalamulitsa, komabe muchitepo kanthu kuti dzina lanu lisanyozeke. Kusakhulupirika kwathu nkwakukuludi. Takuchimwirani zedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anthu akuti, “Ngakhale machimo athu akutitsutsa, koma Inu Yehova chitanipo kanthu chifukwa cha dzina lanu. Pakuti kusakhulupirika kwathu nʼkwakukulu; ife takuchimwirani. Onani mutuwo |