Yeremiya 14:18 - Buku Lopatulika18 Ndikatulukira kumunda, taonani ophedwa ndi lupanga! Ndikalowa m'mzinda, taonani odwala ndi njala! Pakuti mneneri ndi wansembe ayendayenda m'dziko osadziwa kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndikatulukira kumunda, taonani ophedwa ndi lupanga! Ndikalowa m'mudzi, taonani odwala ndi njala! Pakuti mneneri ndi wansembe ayendayenda m'dziko osadziwa kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndikamayenda ku thengo, ndikuwona anthu ophedwa pa nkhondo. Ndikaloŵa mu mzinda, ndikuwona anthu ofa ndi njala. Aneneri ndi ansembe akupitirizabe ntchito zao m'dzikomo, koma osadziŵa zimene akuchita.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndikapita kuthengo, ndikuona amene aphedwa ndi lupanga; ndikapita mu mzinda, ndikuona amene asakazidwa ndi njala. Ngakhale aneneri pamodzi ndi ansembe onse atengedwa.’ ” Onani mutuwo |