Yeremiya 14:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Yehova anati kwa ine, Usapempherere anthu awa zabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Yehova anati kwa ine, Usapempherere anthu awa zabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pambuyo pake Chauta adandiwuza kuti, “Usaŵapempherere anthu ameneŵa, kuŵafunira zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Usawapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino. Onani mutuwo |