Yeremiya 13:26 - Buku Lopatulika26 Chifukwa chake Ine ndidzaonetsa zotopola mikawo zako, pamaso pako, ndipo manyazi ako adzaoneka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Chifukwa chake Ine ndidzaonetsa zotopola mikawo zako, pamaso pako, ndipo manyazi ako adzaoneka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 “Ine Chauta ndidzakwinza zovala zanu mpaka kumaso, ndipo maliseche anu adzaoneka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ine ndidzakwinya zovala zanu mpaka ku maso kuti umaliseche wanu uwonekere. Onani mutuwo |