Yeremiya 13:25 - Buku Lopatulika25 Ichi ndi chogwera chako, gawo la muyeso wako wa kwa Ine, ati Yehova; chifukwa wandiiwala Ine, ndi kukhulupirira zonama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ichi ndi chogwera chako, gawo la muyeso wako wa kwa Ine, ati Yehova; chifukwa wandiiwala Ine, ndi kukhulupirira zonama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Zokuyenerani nzimenezi, chilango chimene ndakukonzerani chifukwa choti mwandiiŵala, mwakhala mukudalira milungu yonama,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Limeneli ndiye gawo lanu, chilango chimene ndakukonzerani chifukwa chondiyiwala Ine ndi kutumikira milungu yabodza, akutero Yehova. Onani mutuwo |