Yeremiya 13:24 - Buku Lopatulika24 Chifukwa chake ndidzabalalitsa iwo, monga ziputu zakupita, ndi mphepo ya kuchipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Chifukwa chake ndidzabalalitsa iwo, monga ziputu zakupita, ndi mphepo ya kuchipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Chifukwa cha kuipa kwanuko, ndidzakumwazani ngati mankhusu, onka nauluka ndi mphepo yakuchipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Ine ndidzakumwazani ngati mankhusu amene amawuluka ndi mphepo ya ku chipululu. Onani mutuwo |