Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 13:23 - Buku Lopatulika

23 Kodi angathe Mkusi kusanduliza khungu lake, kapena nyalugwe mawanga ake? Pamenepo mungathe inunso kuchita zabwino, inu amene muzolowera kuchita zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Kodi angathe Mkusi kusanduliza khungu lake, kapena nyalugwe mawanga ake? Pamenepo mungathe inunso kuchita zabwino, inu amene muzolowera kuchita zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Kodi munthu wakuda nkusintha khungu lake? Kodi kambuku nkusintha maŵanga ake? Ndiye kuti inuyo, ozoloŵera kuchimwanu, mungathe kumachita zabwino ngati?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Kodi wa dziko la Kusi nʼkusintha khungu lake, kapena kambuku kusintha mawanga ake? Inunso amene munazolowera kuchita zoyipa simungathe kusintha.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 13:23
13 Mawu Ofanana  

Koma sanamvere, nachita monga mwa mwambo wao woyamba.


Ungakhale ukonola chitsiru m'mtondo ndi munsi, pamodzi ndi mphale, koma utsiru wake sudzamchoka.


Chokhotakhota sichingaongokenso; ndipo choperewera sichingawerengedwe.


Nanga bwanji mukali chimenyedwere kuti inu mulikupandukirabe? Mutu wonse ulikudwala, ndi mtima wonse walefuka.


Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa?


Pakuti ngakhale usamba ndi soda, ndi kudzitengera sopo wambiri, mphulupulu zako zidziwika pamaso panga, ati Yehova Mulungu.


Ndapanda ana anu mwachabe; sanamvere kulanga; lupanga lanu ladya aneneri anu, monga mkango wakuononga.


Pakuti anthu anga apusa, sandidziwa Ine; ali ana opulukira sazindikira; ali ochenjera kuchita choipa koma kuchita chabwino sakudziwa.


Yehova Inu, maso anu sali pachoonadi kodi? Munawapanda iwo, koma sanaphwetekedwe mtima; munawatha iwo, koma akana kudzudzulidwa; alimbitsa nkhope zao koposa mwala; akana kubwera.


Ndipo yense adzanyenga mnansi wake, osanena choonadi; aphunzitsa lilime lao kunena zonama; nadzithodwetsa kuchita zoipa.


Ndipo pamene anauza Saulo, iye anatumiza mithenga ina; koma iyonso inanenera. Ndipo Saulo anatumiza mithenga kachitatu, nayonso inanenera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa