Yeremiya 13:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo ngati udzati m'mtima mwako, Zimenezi zandifikira ine chifukwa ninji? Chifukwa cha choipa chako chachikulu nsalu zako zoyesa mfula zasanduka mbudulira, ndi zitendene zako zaphwetekwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo ngati udzati m'mtima mwako, Zimenezi zandifikira ine chifukwa ninji? Chifukwa cha choipa chako chachikulu nsalu zako zoyesa mfula zasanduka mbudulira, ndi zithende zako zaphwetekwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mukamadzifunsa kuti, ‘Kodi zimenezi zatigwera bwanji?’ Nchifukwa cha machimo anu ambiri kuti zovala zanu zikwinzidwe, ndipo kuti akuchiteni zankhanza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndipo ngati udzadzifunsa kuti, “Kodi zimenezi zandichitikira chifukwa chiyani?” Ndi chifukwa cha machimo anu ambiri kuti zovala zanu zingʼambike ndiponso kuti akuchitireni nkhanza. Onani mutuwo |