Yeremiya 13:21 - Buku Lopatulika21 Udzanena chiyani pamene adzaika abale ako kukhala akulu ako, pakuti iwe wekha wawalangiza iwo akukana iwe? Kodi zowawa sizidzakugwira iwe monga mkazi wobala? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Udzanena chiyani pamene adzaika abale ako akulu ako, pakuti iwe wekha wawalangiza iwo akukana iwe? Kodi zowawa sizidzakugwira iwe monga mkazi wobala? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Kodi mudzatani akadzakuikirani kuti azikulamulirani anthu amene munkaŵayesa abwenzi anu? Kodi simudzamva zoŵaŵa zonga za mkazi pa nthaŵi yochira? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kodi udzanena chiyani pamene [Yehova] adzakuyikira anthu amene unkanena kuti ndi abale ako akukugonjetsa ndi kukulamulira? Kodi sudzamva zowawa ngati za mayi pa nthawi yake yochira? Onani mutuwo |