Yeremiya 13:18 - Buku Lopatulika18 Nenani kwa mfumu ndi kwa amake wa mfumu, Dzichepetseni, khalani pansi; pakuti zapamtu zanu zagwa, korona wanu wokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Nenani kwa mfumu ndi kwa amake wa mfumu, Dzichepetseni, khalani pansi; pakuti zapamtu zanu zagwa, korona wanu wokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Uza mfumu pamodzi ndi mai wake kuti, “Tsikani pa mipando yaufumu, poti zisoti zanu zokongola zaufumu zagwa pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Uza mfumu pamodzi ndi amayi ake kuti, “Tsikani pa mipando yaufumuyo, pakuti zipewa zanu zaufumu zokongolazo zagwa pansi.” Onani mutuwo |