Yeremiya 13:17 - Buku Lopatulika17 Koma ngati simudzamva, moyo wanga udzalira m'tseri chifukwa cha kunyada kwanu; diso langa lidzalira kwambiri, lidzagwa misozi, chifukwa zoweta za Yehova zagwidwa m'nsinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma ngati simudzamva, moyo wanga udzalira m'tseri chifukwa cha kunyada kwanu; diso langa lidzalira kwambiri, lidzagwa misozi, chifukwa zoweta za Yehova zagwidwa m'nsinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma mukapanda kumvera, mtima wanga udzalira m'seri chifukwa cha kunyada kwanu. M'maso mwanga mudzadzaza misozi yoŵaŵa chifukwa choti nkhosa za Chauta zatengedwa ukapolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma ngati simumvera, ndidzalira kwambiri chifukwa cha kunyada kwanu. Mʼmaso mwanga mwadzaza ndi misozi yowawa chifukwa nkhosa za Yehova zatengedwa ukapolo. Onani mutuwo |