Yeremiya 12:9 - Buku Lopatulika9 Cholowa changa chili kwa ine ngati mbalame yamawalamawala yolusa? Kodi mbalame zolusa zimzinga ndi kudana naye? Mukani, musonkhanitse zilombo za m'thengo, mudze nazo zidye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Cholowa changa chili kwa ine ngati mbalame yamawalamawala yolusa? Kodi mbalame zolusa zimzinga ndi kudana naye? Mukani, musonkhanitse zilombo za m'thengo, mudze nazo zidye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Anthu anga osankhidwa ali ngati mbalame yamaŵangamaŵanga imene akabaŵi aizinga kuchokera konsekonse. Kasonkhanitseni nyama zakuthengo, mubwere nazo ku phwando. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anthu anga amene ndinawasankha asanduka ngati mbalame yolusa yamawangamawanga imene akabawi ayizinga. Pitani, kasonkhanitseni nyama zakuthengo. Mubwere nazo kuti zidzadye mbalameyo. Onani mutuwo |