Yeremiya 12:7 - Buku Lopatulika7 Ndachoka kunyumba yanga, ndasiya cholowa changa; ndapereka wokondedwa wa mtima wanga m'dzanja la adani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndachoka kunyumba yanga, ndasiya cholowa changa; ndapereka wokondedwa wa mtima wanga m'dzanja la adani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Banja la Israele ndalisiya, ndaŵataya anthu amene ndidaŵasankha. Okondeka anga ndaŵapereka kwa adani ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Ine ndawasiya anthu anga; anthu amene ndinawasankha ndawataya. Ndapereka okondedwa anga mʼmanja mwa adani awo. Onani mutuwo |