Yeremiya 12:13 - Buku Lopatulika13 Abzala tirigu, asenga minga; adzipweteka, koma osapindula kanthu, mudzakhala ndi manyazi a zipatso zanu, chifukwa cha mkwiyo woopsa wa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Abzala tirigu, asenga minga; adzipweteka, koma osapindula kanthu, mudzakhala ndi manyazi a zipatso zanu, chifukwa cha mkwiyo woopsa wa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Anthu adafesa tirigu, koma adakolola minga. Adadzitopetsa pogwira ntchito, koma osapindula nkanthu komwe. Zokolola zao nzochititsa manyazi, chifukwa cha mkwiyo woopsa wa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Anthu anafesa tirigu koma anatuta minga; anadzitopetsa kugwira ntchito koma osapeza phindu lililonse. Choncho mudzachita manyazi ndi zokolola zanu chifukwa cha mkwiyo wa Yehova.” Onani mutuwo |