Yeremiya 12:12 - Buku Lopatulika12 Akufunkha afika pa mapiri oti see m'chipululu; pakuti lupanga la Yehova lilusa kuyambira pa mbali ina ya dziko kufikira kumbali ina; palibe thupi lokhala ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Akufunkha afika pa mapiri oti see m'chipululu; pakuti lupanga la Yehova lilusa kuyambira pa mbali ina ya dziko kufikira kumbali ina; palibe thupi lokhala ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu oononga abalalikira ku zitunda zonse zam'chipululu. Ndipo Ine Chauta ndatuma ankhondo kuti akanthe dziko lonse, kuyambira ku malire ena mpaka ku malire enanso. Palibe aliyense amene angapeze mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu onse owononga abalalikira ku zitunda zonse za mʼchipululu. Yehova watuma ankhondo ake kudzawatha kuyambira kumalire ena a dziko mpaka ku malire enanso a dziko, ndipo palibe amene adzakhale pa mtendere. Onani mutuwo |