Yeremiya 12:10 - Buku Lopatulika10 Abusa ambiri aononga munda wanga wampesa, apondereza gawo langa, pondikondweretsa apayesa chipululu chopanda kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Abusa ambiri aononga munda wanga wamphesa, apondereza gawo langa, pondikondweretsa apayesa chipululu chopanda kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Abusa ambiri adaononga munda wanga wamphesa, adapondereza munda wanga. Munda wokoma uja adausandutsa chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Abusa ambiri anawononga munda wanga wa mpesa, anapondereza munda wanga; munda wanga wabwino uja anawusandutsa chipululu. Onani mutuwo |
taonani, Ine, ndidzatuma ndi kutenga mabanja onse a kumpoto, ati Yehova, ndipo ndidzatuma kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga, ndipo ndidzatengera iwo padziko lino, ndi pa okhalamo ake onse, ndi pa mitundu iyi yozungulira, ndipo ndidzathetsa iwo ndithu, ndi kuwayesa iwo chizizwitso, ndi chotsonyetsa, ndi bwinja lamuyaya.