Yeremiya 11:20 - Buku Lopatulika20 Koma, Yehova wa makamu, amene aweruza molungama, amene ayesa impso ndi mtima, ndikuoneni Inu mulikuwabwezera chilango, pakuti kwa Inu ndawulula mlandu wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma, Yehova wa makamu, amene aweruza molungama, amene ayesa impso ndi mtima, ndikuoneni Inu mulikuwabwezera chilango, pakuti kwa Inu ndawulula mlandu wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Inu Chauta Wamphamvuzonse amene mumaweruza molungama, amene mumayesa mtima ndi maganizo, onetseni kuti mwaŵalipsira, pajatu ndidadzipereka m'manja mwanu! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma, Inu Yehova Wamphamvuzonse, Inu amene mumaweruza molungama ndi kuyesa mitima ndi maganizo, lolani kuti ine ndione kuti mwawalipsira, pakuti mlandu wanga ndawupereka mʼmanja mwanu. Onani mutuwo |