Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 11:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo Yehova anandidziwitsa, ndipo ndinadziwa; ndipo wandisonyeza ine machitidwe ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo Yehova anandidziwitsa, ndipo ndinadziwa; ndipo wandisonyeza ine machitidwe ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Chauta adandiwululira, ndipo ndidadziŵa za chiwembu cha anthu. Iye adatsekula maso anga nandiwonetsa ntchito zao zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Yehova anandiwululira ndipo ndinadziwa. Iye anatsekula maso anga kuti ndione chiwembu chawocho.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 11:18
8 Mawu Ofanana  

Koma Elisa anakhala pansi m'nyumba mwake, ndi akulu anakhala pansi pamodzi naye; ndipo mfumu inatuma munthu amtsogolere, koma asanafike kwa Elisa mthengayo, anati kwa akulu, Mwapenya kodi m'mene mwana uyu wambanda watumiza munthu kuchotsa mutu wanga? Taonani, pakufika mthengayo mutseke pakhomo, mumkankhe ndi chitseko. Kodi mapazi a mbuye wake samveka dididi pambuyo pake?


Koma ine ndinanga mwanawankhosa wofatsa wotengedwa kukaphedwa; ndipo sindinadziwe kuti anandichitira ine chiwembu, kuti, Tiononge mtengo ndi zipatso zake, timdule iye padziko la amoyo, kuti dzina lake lisakumbukikenso.


Ndipo munthu akanena kanthu ndi inu, mudzati, Ambuye asowa iwo, ndipo pomwepo adzawatumiza.


Pakuti ngati choonadi cha Mulungu chichulukitsa ulemerero wake chifukwa cha bodza langa, nanga inenso ndiweruzidwa bwanji monga wochimwa?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa