Yeremiya 11:16 - Buku Lopatulika16 Yehova anatcha dzina lako, Mtengo wa azitona wauwisi, wokoma wa zipatso zabwino; ndi mau a phokoso lalikulu wayatsa moto pamenepo, ndipo nthambi zake zathyoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Yehova anatcha dzina lako, Mtengo wa azitona wauwisi, wokoma wa zipatso zabwino; ndi mau a phokoso lalikulu wayatsa moto pamenepo, ndipo nthambi zake zathyoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kale Chauta ankakuyerekezani ndi mtengo wa olivi wa masamba obiriŵira ndi wa zipatso zokongola. Koma tsopano adzautentha ndi mkuntho wamkokomo, ndipo nthambi zake zidzapserera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kale Yehova ankakutchani mtengo wa olivi wa masamba obiriwira, wokhala ndi zipatso zokongola. Koma tsopano adzawutentha ndi mkuntho wamkokomo ndipo nthambi zake zidzapserera. Onani mutuwo |