Yeremiya 10:24 - Buku Lopatulika24 Yehova, mundilangize, koma ndi chiweruzo; si m'mkwiyo wanu, mungandithe psiti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Yehova, mundilangize, koma ndi chiweruzo; si m'mkwiyo wanu, mungandithe psiti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Langizeni, Inu Chauta, koma mwachilungamo. Musandikwiyire kuti mungandiwononge. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Inu Yehova, langizeni, komatu mwachilungamo, osati ndi mkwiyo wanu, mungandiwononge kotheratu. Onani mutuwo |