Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 10:23 - Buku Lopatulika

23 Inu Yehova, ndidziwa kuti njira ya munthu sili mwa iye mwini; sikuli kwa munthu woyenda kulongosola mapazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Inu Yehova, ndidziwa kuti njira ya munthu sili mwa iye mwini; sikuli kwa munthu woyenda kulongosola mapazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Inu Chauta, ndikudziŵa kuti moyo umene ali nawo munthu si wake. Munthu sangathe kudzitsogolera yekha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Inu Yehova, ndikudziwa kuti moyo umene munthu ali nawo si wake; munthuyo sangathe kuwongolera mayendedwe ake.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 10:23
9 Mawu Ofanana  

M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Yehova akhazikitsa mayendedwe a munthu; ndipo akondwera nayo njira yake.


Malongosoledwe a mtima nga munthu; koma mayankhidwe a lilime achokera kwa Yehova.


Mtima wa munthu ulingalira njira yake; koma Yehova ayendetsa mapazi ake.


Yehova alongosola mayendedwe a mwamuna; munthu tsono angazindikire bwanji njira yake?


umlemekeze m'njira zako zonse, ndipo Iye adzaongola mayendedwe ako.


Njira ya wolungama ili njira yoongoka; Inu amene muli woongoka, mukonza njira ya wolungama.


koma munadzikweza kutsutsana naye Ambuye wa Kumwamba; ndipo anabwera nazo zotengera za nyumba yake kwa inu; ndi inu ndi akulu anu, akazi anu ndi akazi anu aang'ono, mwamweramo vinyo; mwalemekezanso milungu yasiliva, ndi yagolide, yamkuwa, yachitsulo, yamtengo, ndi yamwala, imene siiona kapena kumva, kapena kudziwa; ndi Mulungu amene m'dzanja mwake muli mpweya wanu, ndi njira zanu zonse, yemweyo simunamchitire ulemu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa