Yeremiya 10:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti abusa apulukira, sanafunsire kwa Yehova; chifukwa chake sanapindule; zoweta zao zonse zabalalika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti abusa apulukira, sanafunsire kwa Yehova; chifukwa chake sanapindule; zoweta zao zonse zabalalika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Paja abusa ndi opusa, sapempha nzeru kwa Chauta. Nchifukwa chake zinthu sizidaŵayendere bwino, ndipo nkhosa zao zidabalalika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Abusa ndi opusa ndipo sanapemphe nzeru kwa Yehova; choncho palibe chimene anapindula ndipo nkhosa zawo zonse zabalalika. Onani mutuwo |