Yeremiya 10:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti atero Yehova, Taonani, ndidzaponya kunja okhala m'dziko ili tsopanoli, ndi kuwasautsa, kuti azindikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti atero Yehova, Taonani, ndidzaponya kunja okhala m'dziko ili tsopanoli, ndi kuwasautsa, kuti azindikire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta akunena kuti, “Tsopano ndichotsa anthu onse a m'dziko lino. Ndidzaŵagwetsa m'mavuto, mpaka aŵamve ndithu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti Yehova akuti, “Tsopano Ine ndidzachotsa anthu onse amene akukhala mʼdziko lino; adzakhala pa mavuto mpaka adzamvetsa.” Onani mutuwo |