Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 10:17 - Buku Lopatulika

17 Nyamula katundu wako, iwe wokhala m'linga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Nyamula katundu wako, iwe wokhala m'linga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Tolatolani katundu wanu, osamsiyanso pansi, inu amene adani akuzingani ndi zithando zankhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Sonkhanitsani katundu wanu, inu amene mukukhala mʼlinga la ankhondo.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 10:17
6 Mawu Ofanana  

Taonani, Ine ndine mdani wako, iwe wokhala m'chigwa, ndi pa thanthwe la m'chidikha, ati Yehova; inu amene muti, Ndani adzatsikira kumenyana ndi ife? Ndani adzalowa m'zokhalamo zathu?


Ananu a Benjamini, pulumukani pothawa pakati pa Yerusalemu, ombani lipenga mu Tekowa, kwezani chizindikiro mu Betehakeremu; pakuti chaoneka choipa chotuluka m'mpoto ndi kuononga kwakukulu.


Nyamukani, chokani, pakuti popumula panu si pano ai; chifukwa cha udyo wakuononga ndi chionongeko chachikulu.


Chifukwa chake m'mene mukadzaona chonyansa cha kupululutsa, chimene chidanenedwa ndi Daniele mneneri, chitaima m'malo oyera (iye amene awerenga m'kalata azindikire)


Ndipo adzakuzingani m'midzi mwanu monse, kufikira adzagwa malinga anu aatali ndi olimba, amene munawakhulupirira, m'dziko lanu lonse; inde, adzakuzingani m'midzi mwanu monse, m'dziko lanu lonse limene Yehova Mulungu wanu akupatsani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa