Yeremiya 10:15 - Buku Lopatulika15 Ndiwo chabe, ndiwo chiphamaso; pa nthawi ya kulangidwa kwao adzatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndiwo chabe, ndiwo chiphamaso; pa nthawi ya kulangidwa kwao adzatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mafanowo ngachabechabe, ayenera kuŵaseka, ndipo pamene anthuwo adzalangidwe, mafanowo adzaonongeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo. Pamene anthuwo azidzaweruzidwa, mafanowo adzawonongedwa. Onani mutuwo |