Yeremiya 1:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo adzamenyana ndi iwe; koma sadzakuposa; chifukwa Ine ndili ndi iwe, ati Yehova, kukulanditsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo adzamenyana ndi iwe; koma sadzakuposa; chifukwa Ine ndili ndi iwe, ati Yehova, kukulanditsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iwo adzalimbana nawe, koma sadzakupambana, pakuti ine ndili nawe ndipo ndidzakupulumutsa,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Iwo adzalimbana nawe koma sadzakugonjetsa, popeza Ine ndili nawe ndipo ndidzakupulumutsa,” akutero Yehova. Onani mutuwo |