Yeremiya 1:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Yehova anati kwa ine, Kuchokera kumpoto choipa chidzatulukira onse okhala m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Yehova anati kwa ine, Kuchokera kumpoto choipa chidzatulukira onse okhala m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Apo Iye adandiwuza kuti, “Ndiye kuti tsoka la anthu a m'dziko lino lidzachokera kumpoto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yehova anandiwuza kuti, “Mavuto a anthu onse okhala mʼdziko lino adzachokera kumpoto. Onani mutuwo |
taonani, Ine, ndidzatuma ndi kutenga mabanja onse a kumpoto, ati Yehova, ndipo ndidzatuma kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga, ndipo ndidzatengera iwo padziko lino, ndi pa okhalamo ake onse, ndi pa mitundu iyi yozungulira, ndipo ndidzathetsa iwo ndithu, ndi kuwayesa iwo chizizwitso, ndi chotsonyetsa, ndi bwinja lamuyaya.