Yakobo 4:3 - Buku Lopatulika3 Mupempha, ndipo simulandira, popeza mupempha koipa, kuti mukachimwaze pochita zikhumbitso zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mupempha, ndipo simulandira, popeza mupempha koipa, kuti mukachimwaze pochita zikhumbitso zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndipo ngakhale mupemphe, simulandira, chifukwa mumapempha molakwa. Zimene mumapempha, mumafuna kungozimwazira pa zokukondweretsani basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma ngakhale mumapempha simulandira, chifukwa mumapempha ndi zolinga zoyipa. Mumapempha kuti muzigwiritse ntchito pa zokusangalatsani nokha. Onani mutuwo |