Yakobo 3:14 - Buku Lopatulika14 Koma mukakhala nako kaduka kowawa, ndi chotetana m'mtima mwanu, musadzitamandira, ndipo musamanama potsutsana nacho choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma mukakhala nako kaduka kowawa, ndi chotetana m'mtima mwanu, musadzitamandira, ndipo musamanama potsutsana nacho choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma ngati muli ndi mtima wakaduka ndi wodzikonda, musamanyada ndi kutsutsana ndi choona pakunena mabodza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma ngati muli ndi mtima wakaduka ndi odzikonda, musadzitamandire kapena kukana choonadi. Onani mutuwo |