Yakobo 2:24 - Buku Lopatulika24 Mupenya kuti munthu ayesedwa wolungama ndi ntchito yake, osati ndi chikhulupiriro chokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Mupenya kuti munthu ayesedwa wolungama ndi ntchito yake, osati ndi chikhulupiriro chokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mukuwonatu kuti zochita zake za munthu ndizo zimamsandutsa wolungama pamaso pa Mulungu, osati chikhulupiriro chokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Tsono mukuona kuti munthu amasanduka wolungama ndi ntchito zabwino osati ndi chikhulupiriro chokha ayi. Onani mutuwo |